Amosi 4:9 - Buku Lopatulika9 Ndinakukanthani ndi chinsikwi ndi chinoni; minda yanu yochuluka yamipesa, ndi yamikuyu, ndi ya azitona, yaonongeka ndi dzombe; koma simunabwerere kudza kwa Ine, ati Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndinakukanthani ndi chinsikwi ndi chinoni; minda yanu yochuluka yamipesa, ndi yamikuyu, ndi ya azitona, yaonongeka ndi dzombe; koma simunabwerera kudza kwa Ine, ati Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 “Ndidaumitsa mbeu zanu ndi matenda ndiponso ndi chinoni. Chidafotetsa mbeu za m'minda yanu yonse ndi yamphesa yomwe. Dzombe lidaononga mikuyu yanu ndi mitengo ya olivi, komabe simudabwerere kwa Ine.” Akutero Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 “Nthawi zambiri ndinakantha mbewu zanu ndiponso minda ya mpesa, ndinayikantha ndi chinsikwi ndiponso ndi chiwawu. Dzombe linawononga mikuyu yanu ndi mitengo ya olivi. Komabe inu simunabwerere kwa Ine,” akutero Yehova. Onani mutuwo |