Amosi 3:9 - Buku Lopatulika9 Bukitsani kunyumba zachifumu za Asidodi, ndi kunyumba zachifumu za m'dziko la Ejipito, nimuziti, Sonkhanani pa mapiri a Samariya, ndipo penyani masokosero aakulu m'menemo, ndi ozunzika m'kati mwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Bukitsani kunyumba zachifumu za Asidodi, ndi kunyumba zachifumu za m'dziko la Ejipito, nimuziti, Sonkhanani pa mapiri a Samariya, ndipo penyani masokosero akulu m'menemo, ndi ozunzika m'kati mwake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 “Ulengeze kwa anthu okhala m'malinga a ku Asidodi, ndiponso kwa okhala m'malinga a ku Ejipito, uŵauze kuti akasonkhane ku mapiri a ku Samariya, akaone zachipwirikiti ndi zachifwamba zimene zikuchitika pakati pa anthu ake.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Lengezani zimenezi ku nyumba zaufumu za ku Asidodi ndiponso ku nyumba zaufumu za ku Igupto: “Sonkhanani ku mapiri a ku Samariya; onani chisokonezo pakati pake ndiponso kuponderezana pakati pa anthu ake.” Onani mutuwo |