Amosi 3:8 - Buku Lopatulika8 Mkango ukabangula, ndani amene saopa? Ambuye Yehova wanena, ndani amene sanenera? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Mkango ukabangula, ndani amene saopa? Ambuye Yehova wanena, ndani amene sanenera? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Mkango ukabangula, kodi sachita mantha ndani? Ambuye Chauta akalankhula, kodi ndani sadzalalika?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Mkango wabangula, ndani amene sachita mantha? Ambuye Yehova wayankhula, ndani amene sanganenere? Onani mutuwo |