Amosi 3:10 - Buku Lopatulika10 Pakuti sadziwa kuchita zolungama, amene akundika zachiwawa ndi umbala m'nyumba zao zachifumu, ati Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Pakuti sadziwa kuchita zolungama, amene akundika zachiwawa ndi umbala m'nyumba zao zachifumu, ati Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 “Sadziŵa kuchita zolungama amene amadzaza malinga ao ndi zinthu zozipeza mwankhondo ndi mwakuba.” Akuterotu Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 “Iwo sadziwa kuchita zolungama, ndipo amadzaza malo awo otetezedwa ndi zinthu zolanda ku nkhondo ndi zakuba,” akutero Yehova. Onani mutuwo |