Amosi 3:2 - Buku Lopatulika2 Inu nokha ndinakudziwani mwa mabanja onse a padziko lapansi, m'mwemo ndidzakulangani chifukwa cha mphulupulu zanu zonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Inu nokha ndinakudziwani mwa mabanja onse a pa dziko lapansi, m'mwemo ndidzakulangani chifukwa cha mphulupulu zanu zonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Ine ndidasankha ndi kusamala inu nokha pakati pa mitundu yonse ya pa dziko lapansi. Tsono ndidzakulangani koposa chifukwa cha machimo anu onse.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Inu nokha ndi amene ndinakusankhani pakati pa mabanja onse a dziko lapansi; nʼchifukwa chake ndidzakulangani chifukwa cha machimo anu onse.” Onani mutuwo |