Amosi 3:1 - Buku Lopatulika1 Tamverani mau awa akunenerani Yehova motsutsa, inu ana a Israele, kulinenera banja lonse ndinalikweza kulitulutsa m'dziko la Ejipito, ndi kuti, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Tamverani mau awa akunenerani Yehova motsutsa, inu ana a Israele, kulinenera banja lonse ndinalikweza kulitulutsa m'dziko la Ejipito, ndi kuti, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Imvani mau amene Chauta adalankhula, mau okudzudzulani inu Aisraele, ndiye kuti banja lonse limene Iye adalitulutsa ku dziko la Ejipito. Adanena kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Inu Aisraeli, imvani mawu awa amene Yehova wayankhula kutsutsana nanu, kutsutsana ndi banja lonse limene analitulutsa mu Igupto: Onani mutuwo |