Amosi 2:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo ndinakukwezani kuchokera m'dziko la Ejipito, ndi kukutsogolerani zaka makumi anai m'chipululu, kuti mulandire dziko la Aamori likhale cholowa chanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo ndinakukwezani kuchokera m'dziko la Ejipito, ndi kukutsogolerani zaka makumi anai m'chipululu, kuti mulandire dziko la Aamori likhale cholowa chanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Inu Aisraele, ndine ndidakutulutsani ku dziko la Ejipito. Ndine ndidakutsogolerani m'chipululu zaka makumi anai, kuti mukalande dziko la Aamori lija. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 “Ine ndinakutulutsani ku Igupto, ndipo ndinakutsogolerani mʼchipululu kwa zaka makumi anayi, kudzakupatsani dziko la Aamori. Onani mutuwo |