Amosi 2:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo ndinaukitsa mwa ana anu aneneri, ndi mwa anyamata anu Anaziri. Si momwemo, inu ana a Israele, ati Yehova? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo ndinaukitsa mwa ana anu aneneri, ndi mwa anyamata anu Anaziri. Si momwemo, inu ana a Israele, ati Yehova? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Ndipo ndine ndidasankha ena mwa ana anu kuti akhale aneneri, nkusankha ena mwa anyamata anu kuti akhale Anaziri. Kodi si choncho, inu anthu a ku Israele?” Akuterotu Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Ine ndinawutsanso ena mwa ana ako kuti akhale aneneri, ndi ena mwa anyamata ako kuti akhale anaziri. Kodi si choncho, inu Aisraeli?” akutero Yehova. Onani mutuwo |
Ndipo Yehova anachitira umboni Israele ndi Yuda mwa dzanja la mneneri aliyense, ndi mlauli aliyense, ndi kuti, Bwererani kuleka ntchito zanu zoipa, nimusunge malamulo anga ndi malemba anga, monga mwa chilamulo chonse ndinachilamulira makolo anu, ndi kuchitumizira inu mwa dzanja la atumiki anga aneneri.