Amosi 2:9 - Buku Lopatulika9 Koma ndinaononga Ine pamaso pa Aamori, amene msinkhu wao unanga msinkhu wa mikungudza, nakhala nayo mphamvu ngati thundu; koma ndinaononga zipatso zao m'mwamba, ndi mizu yao pansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Koma ndinaononga Ine pamaso pa Aamori, amene msinkhu wao unanga msinkhu wa mikungudza, nakhala nayo mphamvu ngati thundu; koma ndinaononga zipatso zao m'mwamba, ndi mizu yao pansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 “Komabe ndine amene ndidaononga Aamori pamene Aisraele ankafika, ngakhale iwo aja anali ataliatali ngati mikungudza, ngakhale anali amphamvu ngati mitengo ya thundu. Ndidaŵaonongeratu zipatso zao m'mwamba ndiponso mizu yao pansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 “Ine ndinawononga Aamori pamaso pawo, ngakhale iwo anali anthu ataliatali ngati mikungudza ndiponso amphamvu ngati mitengo ya thundu. Ndinawononga zipatso zawo ndiponso mizu yawo. Onani mutuwo |