Amosi 1:6 - Buku Lopatulika6 Atero Yehova, Chifukwa cha zolakwa zitatu za Gaza, kapena zinai, sindidzabweza kulanga kwake; popeza anatenga ndende anthu onse kuwapereka kwa Edomu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Atero Yehova, Chifukwa cha zolakwa zitatu za Gaza, kapena zinai, sindidzabweza kulanga kwake; popeza anatenga ndende anthu onse kuwapereka kwa Edomu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Zimene akunena Chauta ndi izi: “Chifukwa anthu a ku Gaza akunka nachimwirachimwira, sindileka kuŵalanga. Iwo adatenga mtundu wathunthu wa anthu kunka nawo ku ukapolo, ndipo adaupereka ku Edomu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Yehova akuti, “Chifukwa anthu a ku Gaza akunka nachimwirachimwira, Ine sindileka kuwalanga. Popeza anatenga ukapolo mtundu wathunthu ndi kuwugulitsa ku Edomu, Onani mutuwo |