Amosi 1:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo ndidzathyola mpiringidzo wa Damasiko, ndi kulikha okhala m'chigwa cha Aveni, ndi iye wogwira ndodo yachifumu mu Betedeni; ndi anthu a Aramu adzalowa ndende ku Kiri, ati Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo ndidzathyola mpiringidzo wa Damasiko, ndi kulikha okhala m'chigwa cha Aveni, ndi iye wogwira ndodo yachifumu m'Betedeni; ndi anthu a Aramu adzalowa ndende ku Kiri, ati Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ndidzathyola mpiringidzo woteteza mzinda wa Damasiko. Ndidzaonongeratu mfumu yolamulira ku Chigwa cha Aveni, ndiponso iye amene akugwira ndodo yaufumu ku Betedeni. Anthu a ku Siriya adzatengedwa ukapolo kupita nawo ku dziko la Kiri.” Akuterotu Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ndidzathyola chipata cha Damasiko; ndidzawononga mfumu yokhala ku Chigwa cha Aveni, ndiponso iye amene akugwira ndodo yaufumu mu Beti-Edeni. Anthu a ku Aramu adzapita ku ukapolo ku Kiri,” akutero Yehova. Onani mutuwo |