Amosi 1:4 - Buku Lopatulika4 koma ndidzatumiza moto kunyumba ya Hazaele, ndipo udzanyeketsa nyumba zachifumu za Benihadadi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 koma ndidzatumiza moto kunyumba ya Hazaele, ndipo udzanyeketsa nyumba zachifumu za Benihadadi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Tsono Ine ndidzaponya moto pa nyumba ya Hazaele, ndipo motowo udzatentha malinga a Benihadadi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ine ndidzatumiza moto pa nyumba ya Hazaeli umene udzanyeketsa nyumba zaufumu za Beni-Hadadi. Onani mutuwo |