Amosi 1:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo anati, Yehova adzadzuma ali mu Ziyoni, nadzamveketsa mau ake ali mu Yerusalemu; podyetsa abusa padzachita chisoni, ndi mutu wa Karimele udzauma. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo anati, Yehova adzadzuma ali m'Ziyoni, nadzamveketsa mau ake ali m'Yerusalemu; podyetsa abusa padzachita chisoni, ndi mutu wa Karimele udzauma. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Amosi adati, “Chauta akukhuluma ku Ziyoni, mau ake akumveka ngati bingu ku Yerusalemu. Nchifukwa chake mabusa akuuma, msipu wa pa phiri la Karimele ukufota.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Amosi anati: “Yehova akubangula mu Ziyoni ndipo akumveka ngati bingu mu Yerusalemu; msipu wa abusa ukulira, ndipo pamwamba pa Karimeli pakuwuma.” Onani mutuwo |