Amosi 1:14 - Buku Lopatulika14 koma ndidzayatsa moto pa linga la Raba, udzanyeketsa nyumba zachifumu zake, ndi kufuula tsiku la nkhondo, ndi namondwe, tsiku la kamvulumvulu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 koma ndidzayatsa moto pa linga la Raba, udzanyeketsa nyumba zachifumu zake, ndi kufuula tsiku la nkhondo, ndi namondwe, tsiku la kamvulumvulu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Ndiye Ine ndidzaponya moto pa makoma a ku Raba, ndipo motowo udzapsereza malinga ake. Padzakhala kufuula kwakukulu pa tsiku lankhondolo, kumenyana kudzakhala kwafumbi ngati mkuntho wa kamvulumvulu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Ine ndidzayatsa moto pa makoma a ku Raba umene udzanyeketsa nyumba zake zaufumu. Padzakhala kulira kwakukulu pa tsiku la nkhondoyo, kumenyana kudzakhala kwafumbi ngati mkuntho wa kamvuluvulu. Onani mutuwo |