Amosi 1:13 - Buku Lopatulika13 Atero Yehova, Chifukwa cha zolakwa zitatu za ana a Amoni, kapena zinai, sindidzabweza kulanga kwake; popeza anatumbula akazi ali m'pakati a Giliyadi, kuti akuze malire ao; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Atero Yehova, Chifukwa cha zolakwa zitatu za ana a Amoni, kapena zinai, sindidzabweza kulanga kwake; popeza anatumbula akazi ali m'pakati a Giliyadi, kuti akuze malire ao; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Zimene akunena Chauta ndi izi: “Chifukwa Aamoni akunka nachimwirachimwira, sindileka kuŵalanga. Iwo pofuna kufutuza malire ao, adatumbula akazi apakati ku Giliyadi, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Yehova akuti, “Chifukwa anthu a ku Amoni akunka nachimwirachimwira, Ine sindileka kuwalanga. Popeza anatumbula akazi oyembekezera a ku Giliyadi nʼcholinga choti akuze malire awo, Onani mutuwo |