Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Amosi 1:15 - Buku Lopatulika

15 ndipo mfumu yao idzalowa kundende, iyo ndi akalonga ake pamodzi, ati Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 ndipo mfumu yao idzalowa kundende, iyo ndi akalonga ake pamodzi, ati Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Tsono mfumu yao idzatengedwa kunka ku ukapolo, iyoyo pamodzi ndi nduna zake.” Akuterotu Chauta.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Mfumu yawo idzatengedwa kupita ku ukapolo, iyo pamodzi ndi akuluakulu ake,” akutero Yehova.

Onani mutuwo Koperani




Amosi 1:15
2 Mawu Ofanana  

Kuwa, iwe Hesiboni, pakuti Ai wapasuka; lirani, inu ana aakazi a Raba, muvale chiguduli; chitani maliro, thamangani kwina ndi kwina pamipanda; pakuti mfumu yao idzalowa m'ndende, ansembe ake ndi akulu ake pamodzi.


chifukwa chake taona, ndakutambasulira dzanja langa, ndipo ndidzakupereka ukhale chofunkha cha amitundu, ndi kukudula mwa mitundu ya anthu, ndi kukutayikitsa m'maiko, ndidzakuononga; motero udzadziwa kuti Ine ndine Yehova.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa