Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Akolose 4:4 - Buku Lopatulika

4 kuti ndichionetse ichi monga ndiyenera kulankhula.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 kuti ndichionetse ichi monga ndiyenera kulankhula.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Mundipempherere tsono kuti ndichifotokoze bwino monga ndiyenera.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Pempherani kuti ndilalikire momveka bwino, monga ndikuyenera.

Onani mutuwo Koperani




Akolose 4:4
10 Mawu Ofanana  

Ndipo tsopano Ambuye, penyani mau ao akuopsa, ndipo patsani kwa akapolo anu alankhule mau anu ndi kulimbika mtima konse,


Ndipo anayankha Petro ndi atumwi, nati, Tiyenera kumvera Mulungu koposa anthu.


Pokhala nacho tsono chiyembekezo chotere, tilankhula ndi kukhazikika mtima kwakukulu,


chifukwa cha umene ndili mtumiki wa mu unyolo, kuti m'menemo ndikalankhule molimbika, monga ndiyenera kulankhula.


Muyendere munzeru ndi iwo akunja, kuchita machawi nthawi ingatayike.


Mau anu akhale m'chisomo, okoleretsa, kuti mukadziwe inu mayankhidwe anu a kwa yense akatani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa