Akolose 4:17 - Buku Lopatulika17 Ndipo nenani kwa Arkipo, Samaliratu utumiki umene udaulandira mwa Ambuye, kuti uukwanitse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndipo nenani kwa Arkipo, Samaliratu utumiki umene udaulandira mwa Ambuye, kuti uukwanitse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Uzani Arkipo kuti, “Samala bwino kuti ntchito imene Ambuye adakupatsa uziigwira moikapo mtima.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Uzani Arkipo kuti, “Wonetsetsa kuti wamaliza ntchito imene unayilandira mwa Ambuye.” Onani mutuwo |