Akolose 4:1 - Buku Lopatulika1 Ambuye inu, chitirani akapolo anu cholungama ndi cholingana; podziwa kuti inunso muli naye Mbuye mu Mwamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ambuye inu, chitirani akapolo anu cholungama ndi cholingana; podziwa kuti inunso muli naye Mbuye m'Mwamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Inu ambuye, antchito anu muzikhalitsana nawo mwachilungamo ndi moyenera, podziŵa kuti inunso muli ndi Mbuye wanu Kumwamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Mabwana, antchito anu muzikhala nawo mwachilungamo ndi moyenera, podziwa kuti nanunso muli nawo Ambuye anu mmwamba. Onani mutuwo |