Akolose 3:24 - Buku Lopatulika24 podziwa kuti mudzalandira kwa Ambuye mphotho ya cholowa; mutumikira Ambuye Khristu mwaukapolo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 podziwa kuti mudzalandira kwa Ambuye mphotho ya cholowa; mutumikira Ambuye Khristu mwaukapolo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Paja mukudziŵa kuti Ambuye adzakupatsani mphotho. Mphothoyo ndi madalitso amene adalonjeza kudzapatsa anthu ake. Ambuye amene mukuŵatumikirawo ndi Khristu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Inu mukudziwa kuti mudzalandira mphotho monga cholowa kuchokera kwa Ambuye. Ndi Ambuye Khristu amene mukumutumikira. Onani mutuwo |