Akolose 3:23 - Buku Lopatulika23 chilichonse mukachichita, gwirani ntchito mochokera mumtima, monga kwa Ambuye, osati kwa anthu ai; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 chilichonse mukachichita, gwirani ntchito mochokera mumtima, monga kwa Ambuye, osati kwa anthu ai; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Chilichonse chimene mungachite, muchichite ndi mtima wonse, ngati kuti mukuchitira Ambuye, osati anthu ai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Chilichonse mungachite, muchite ndi mtima wanu onse, monga mmene mungagwirire ntchito ya Ambuye osati ya anthu. Onani mutuwo |