Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Akolose 3:19 - Buku Lopatulika

19 Amuna inu, kondani akazi anu, ndipo musawawire mtima iwo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Amuna inu, kondani akazi anu, ndipo musawawire mtima iwo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Inu amuna, muzikonda akazi anu, musamaŵavutitse ai.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Inu amuna, kondani akazi anu ndipo musawapsere mtima.

Onani mutuwo Koperani




Akolose 3:19
14 Mawu Ofanana  

Ndipo Isaki anamlowetsa mkaziyo m'hema wa amake Sara, namtenga Rebeka, nakhala iye mkazi wake; ndipo anamkonda iye; ndipo Isaki anatonthozedwa mtima atafa amake.


Khalani mokondwa ndi mkazi umkonda masiku onse a moyo wako wachabe, umene Mulungu wakupatsa pansi pano masiku ako onse achabe; pakuti ilo ndi gawo lako la m'moyo ndi m'ntchito zimene uvutika nazo pansi pano.


Munthu akadza kwa Ine, wosada atate wake ndi amake, ndi mkazi wake, ndi ana, ndi abale, ndi alongo ake, inde ndi moyo wake womwe wa iye mwini, sangathe kukhala wophunzira wanga.


m'kamwa mwao mudzala ndi zotemberera ndi zowawa;


Chiwawo chonse, ndi kupsa mtima, ndi mkwiyo, ndi chiwawa, ndi mwano zichotsedwe kwa inu, ndiponso choipa chonse.


Amuna inu, kondani akazi anu, monganso Khristu anakonda Mpingo, nadzipereka yekha m'malo mwake;


Komanso inu, yense pa yekha, yense akonde mkazi wake wa iye yekha, monga adzikonda yekha; ndipo mkaziyo akumbukire kuti aziopa mwamuna.


Atate inu, musaputa ana anu, kuti angataye mtima.


Koma mukakhala nako kaduka kowawa, ndi chotetana m'mtima mwanu, musadzitamandira, ndipo musamanama potsutsana nacho choonadi.


Momwemonso amuna inu, khalani nao monga mwa chidziwitso, ndi kuchitira mkazi ulemu, monga chotengera chochepa mphamvu, monganso wolowa nyumba pamodzi wa chisomo cha moyo, kuti mapemphero anu angaletsedwe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa