Ahebri 9:18 - Buku Lopatulika18 momwemo choyambachonso sichinakonzeke chopanda mwazi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 momwemo choyambachonso sichinakonzeka chopanda mwazi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Nchifukwa chake ngakhale Chipangano choyamba chija sichidachitike popanda kukhetsa magazi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Nʼchifukwa chake pangano loyamba lija silinachitike popanda kukhetsa magazi. Onani mutuwo |