Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Ahebri 9:17 - Buku Lopatulika

17 Pakuti chopangiratu chiona mphamvu atafa mwini wake; popeza chilibe mphamvu konse pokhala wolemberayo ali ndi moyo;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Pakuti chopangiratu chiona mphamvu atafa mwini wake; popeza chilibe mphamvu konse pokhala wolemberayo ali ndi moyo;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Paja chipangano chotere chilibe mphamvu, asanamwalire wochilemba. Chimakhala ndi mphamvu pokhapokha wochilembayo atamwalira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 chifukwa pangano lotere limakhala ndi mphamvu ngati wolembayo wamwalira. Siligwira ntchito pamene wolembayo ali ndi moyo.

Onani mutuwo Koperani




Ahebri 9:17
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Israele anati kwa Yosefe, Taona, ndilinkufa ine; Mulungu adzakhala ndi iwe, adzakubwezanso iwe ku dziko la makolo ako.


Mtendere ndikusiyirani inu, mtendere wanga ndikupatsani; Ine sindikupatsani inu monga dziko lapansi lipatsa. Mtima wanu usavutike, kapena usachite mantha.


Abale, ndinena monga munthu. Pangano, lingakhale la munthu, litalunzika, palibe munthu aliyesa chabe, kapena kuonjezapo.


Pakuti pamene pali chopangiratu pafunika pafike imfa ya wolemberayo.


momwemo choyambachonso sichinakonzeke chopanda mwazi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa