Ahebri 8:8 - Buku Lopatulika8 Pakuti powatchulira iwo chifukwa, anena, Taonani, akudza masiku, anena Ambuye, Ndipo ndidzapangana pangano latsopano ndi nyumba ya Israele, ndi nyumba ya Yuda, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Pakuti powatchulira iwo chifukwa, anena, Taonani, akudza masiku, anena Ambuye, Ndipo ndidzapangana pangano latsopano ndi nyumba ya Israele, ndi nyumba ya Yuda, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Koma Mulungu adadzudzula anthu ake ndi mau aŵa akuti, “Masiku akubwera, pamene ndidzachita chipangano chatsopano ndi fuko la Israele, ndiponso ndi fuko la Yuda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Koma Mulungu anapeza zolakwika pakati pa anthu ndipo anati, “Masiku akubwera,” akutero Yehova, “pamene ndidzachita pangano latsopano ndi Aisraeli ndiponso nyumba ya Yuda. Onani mutuwo |