Ahebri 8:9 - Buku Lopatulika9 losati longa pangano ndinalichita ndi makolo ao, tsikuli ndinawagwira kudzanja iwo kuwatsogolera atuluke m'dziko la Ejipito; kuti iwo sanakhalebe m'pangano langa, ndipo Ine sindinawasamalire iwo, anena Ambuye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 losati longa pangano ndinalichita ndi makolo ao, tsikuli ndinawagwira kudzanja iwo kuwatsogolera atuluke m'dziko la Ejipito; kuti iwo sanakhalabe m'pangano langa, ndipo Ine sindinawasamalira iwo, anena Ambuye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Sichidzakhala chonga chipangano chimene ndidaachita ndi makolo ao tsiku limene ndidaachita kuŵagwira pa dzanja kuti ndiŵatulutse m'dziko la Ejipito. Chifukwa iwo sadasunge chipangano changa chija, nanenso sindidaŵasamale”, akutero Ambuye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Silidzakhala ngati pangano limene ndinachita ndi makolo awo, pamene ndinawagwira padzanja nʼkuwatulutsa ku Igupto chifukwa iwo sanasunge pangano langa lija ndipo Ine sindinawasamalire, akutero Ambuye. Onani mutuwo |