Ahebri 8:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo Iye akadakhala padziko, sakadakhala konse wansembe, popeza pali iwo akupereka mitulo monga mwa lamulo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo Iye akadakhala padziko, sakadakhala konse wansembe, popeza pali iwo akupereka mitulo monga mwa lamulo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Iyeyu akadakhala pa dziko lapansi, sibwenzi ali wansembe konse, popeza kuti alipo kale ansembe amene amapereka mphatso potsata Malamulo a Mose. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ngati iye akanakhala pa dziko lapansi, sakanakhala wansembe pakuti alipo kale anthu amene amapereka mphatso zolembedwa mʼMalamulo. Onani mutuwo |