Ahebri 8:3 - Buku Lopatulika3 Pakuti mkulu wa ansembe aliyense aikidwa kupereka mitulo, ndiponso nsembe; potero nkufunika kuti ameneyo akhale nako kanthunso kakupereka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pakuti mkulu wa ansembe aliyense aikidwa kupereka mitulo, ndiponso nsembe; potero nkufunika kuti ameneyo akhale nako kanthunso kakupereka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Paja mkulu wa ansembe aliyense amaikidwa kuti azipereka mphatso ndi nsembe kwa Mulungu. Motero nkofunika kuti wathunso mkulu wa ansembe onse akhale nkanthu koti apereke. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Mkulu wa ansembe aliyense amasankhidwa kuti azipereka mphatso ndi nsembe kwa Mulungu, ndipo kunali koyenera kuti wansembe wathunso akhale nʼkanthu kopereka. Onani mutuwo |