Ahebri 7:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo iwotu mwa ana a Levi akulandira ntchito yakupereka nsembe, ali nalo lamulo lakuti atenge limodzi la magawo khumi kwa anthu monga mwa chilamulo, ndiko kwa abale ao, angakhale adatuluka m'chuuno cha Abrahamu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo iwotu mwa ana a Levi akulandira ntchito yakupereka nsembe, ali nalo lamulo lakuti atenge limodzi la magawo khumi kwa anthu monga mwa chilamulo, ndiko kwa abale ao, angakhale adatuluka m'chuuno cha Abrahamu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Malamulo a Mose amati ana a Levi, amene ali ansembe, azilandira chachikhumi kwa Aisraele. Ndiye kuti iwo amalandira kwa abale ao, ngakhale abalewo nawonso ndi ana a Abrahamu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Tsono lamulo likuti, ana a Levi amene amakhala ansembe azilandira chakhumi kuchokera kwa Aisraeli, abale awo ngakhale kuti abale awowo ndi ochokera kwa Abrahamu. Onani mutuwo |