Ahebri 7:19 - Buku Lopatulika19 (pakuti chilamulo sichinachitire kanthu kakhale kopanda chilema), ndipo kulinso kulowa nacho chiyembekezo choposa, chimene tiyandikira nacho kwa Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 (pakuti chilamulo sichinachitira kanthu kakhale kopanda chilema), ndipo kulinso kulowa nacho chiyembekezo choposa, chimene tiyandikira nacho kwa Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Pajatu Malamulo a Mose sankatha kusandutsa munthu kuti akhale wangwiro. Koma m'malo mwake mwaloŵa chiyembekezo choposa, ndipo mwa chiyembekezo chimenechi timayandikira kwa Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Tsono Malamulo sangathe kusandutsa chilichonse kukhala changwiro, koma mʼmalo mwake mwalowa chiyembekezo chabwino, chimenechi timayandikira nacho kwa Mulungu. Onani mutuwo |
koma podziwa kuti munthu sayesedwa wolungama pa ntchito ya lamulo, koma mwa chikhulupiriro cha Yesu Khristu, ifedi tinakhulupirira kwa Khristu Yesu, kuti tikayesedwe olungama ndi chikhulupiriro cha Khristu, ndipo si ndi ntchito za lamulo; pakuti palibe munthu adzayesedwa wolungama ndi ntchito za lamulo.