Ahebri 7:20 - Buku Lopatulika20 Ndipo monga momwe sikudachitike kopanda lumbiro; (pakuti iwotu anayesedwa ansembe kopanda lumbiro; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ndipo monga momwe sikudachitika kopanda lumbiro; (pakuti iwotu anayesedwa ansembe kopanda lumbiro; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Chinanso nchakuti Mulungu adaachita kulumbira. Amene ankaloŵa unsembe kale lija ankatenga udindo waowo popanda lumbiro. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Izi sizinachitiketu wopanda lumbiro. Ena ankakhala ansembe popanda lumbiro. Onani mutuwo |