Ahebri 7:17 - Buku Lopatulika17 pakuti amchitira umboni, Iwe ndiwe wansembe nthawi yosatha monga mwa dongosolo la Melkizedeki. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 pakuti amchitira umboni, Iwe ndiwe wansembe nthawi yosatha monga mwa dongosolo la Melkizedeki. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Paja mau a Mulungu pomuchitira umboni akuti, “Ndiwe wansembe mpaka muyaya, unsembe wake wonga uja wa Melkizedeki.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Pakuti Mulungu anamuchitira umboni kuti, “Iwe ndi wansembe wamuyaya, monga mwa dongosolo la unsembe wa Melikizedeki.” Onani mutuwo |