Ahebri 7:16 - Buku Lopatulika16 amene wakhala si monga mwa lamulo la lamuliro la kwa thupi, komatu monga mwa mphamvu ya moyo wosaonongeka; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 amene wakhala si monga mwa lamulo la lamuliro la kwa thupi, komatu monga mwa mphamvu ya moyo wosaonongeka; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Iyeyo sadakhale wansembe chifukwa cha malamulo okhudza kubadwa kwa anthu, koma chifukwa cha mphamvu za moyo wake umene uli wosatha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Yesu sanakhale wansembe chifukwa cha malamulo monga mwa mabadwidwe ake koma mwamphamvu ya moyo wosatha. Onani mutuwo |