Ahebri 6:8 - Buku Lopatulika8 koma ikabala minga ndi mitungwi, itayika; nitsala pang'ono ikadatembereredwa; chitsiriziro chake ndicho kutenthedwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 koma ikabala minga ndi mitungwi, itayika; nitsala pang'ono ikadatembereredwa; chitsiriziro chake ndicho kutenthedwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Koma ngati ibereka minga ndi nthula, ndi yachabe ndipo ili pafupi kutembereredwa. Mathero ake nkutenthedwa m'moto. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Koma nthaka yobereka minga ndi nthula ndi yopanda phindu ndipo ili pafupi kutembereredwa. Matsiriziro ake idzatenthedwa mʼmoto. Onani mutuwo |