Ahebri 6:9 - Buku Lopatulika9 Koma, okondedwa, takopeka mtima kuti za inu zili zoposa ndi zophatikana chipulumutso, tingakhale titero pakulankhula; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Koma, okondedwa, takopeka mtima kuti za inu zili zoposa ndi zophatikana chipulumutso, tingakhale titero pakulankhula; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Koma inu okondedwa anga, ngakhale tikunena zimenezi, sitikukukayikirani. Tikudziŵa kuti muli nazo zabwino, zolinga ku chipulumutso chanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Okondedwa anga, ngakhale tikuyankhula zimenezi, ife tikudziwa kuti muli nazo zinthu zabwino zomwe zimabwera pamodzi ndi chipulumutso. Onani mutuwo |