Ahebri 6:7 - Buku Lopatulika7 Pakuti nthaka imene idamwa mvula iigwera kawirikawiri, nipatsa therere loyenera iwo amene adailimira, ilandira dalitso lochokera kwa Mulungu: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Pakuti nthaka imene idamwa mvula iigwera kawirikawiri, nipatsa therere loyenera iwo amene adailimira, ilandira dalitso lochokera kwa Mulungu: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Paja nthaka yolandira mvula kaŵirikaŵiri, nkubereka mbeu zopindulitsa oilima, Mulungu amaidalitsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Nthaka yolandira mvula kawirikawiri nʼkubala mbewu zopindulitsa oyilima, Mulungu amayidalitsa. Onani mutuwo |