Ahebri 6:6 - Buku Lopatulika6 koma anagwa m'chisokero; popeza adzipachikiranso okha Mwana wa Mulungu, namchititsa manyazi poyera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 koma anagwa m'chisokero; popeza adzipachikiranso okha Mwana wa Mulungu, namchititsa manyazi poyera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Tsono akamkana Mulungu tsopano, akuchita ngati kumpachika iwo omwe Mwana wa Mulungu, ndi kumnyozetsa poyera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Popeza anabwerera mʼmbuyo, nʼkosatheka kuti atembenukenso mtima chifukwa akupachikanso Mwana wa Mulungu ndi kumunyozetsa poyera. Onani mutuwo |