Ahebri 6:5 - Buku Lopatulika5 nalawa mau okoma a Mulungu, ndi mphamvu ya nthawi ilinkudza, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 nalawa mau okoma a Mulungu, ndi mphamvu ya nthawi ilinkudza, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ndipo adazindikira kukoma kwa mau a Mulungu, ndi mphamvu za nthaŵi imene inalikudzafika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Analawa kukoma kwa mawu a Mulungu ndi mphamvu za nthawi ikubwera. Onani mutuwo |