Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Ahebri 6:5 - Buku Lopatulika

5 nalawa mau okoma a Mulungu, ndi mphamvu ya nthawi ilinkudza,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 nalawa mau okoma a Mulungu, ndi mphamvu ya nthawi ilinkudza,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Ndipo adazindikira kukoma kwa mau a Mulungu, ndi mphamvu za nthaŵi imene inalikudzafika.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Analawa kukoma kwa mawu a Mulungu ndi mphamvu za nthawi ikubwera.

Onani mutuwo Koperani




Ahebri 6:5
13 Mawu Ofanana  

Talawani, ndipo onani kuti Yehova ndiye wabwino; wodala munthuyo wakukhulupirira Iye.


Ndipo aliyense amene anganenere Mwana wa Munthu zoipa, adzakhululukidwa; koma aliyense amene anganenere Mzimu Woyera zoipa sadzakhululukidwa nthawi ino kapena ilinkudzayo.


pakuti Herode anaopa Yohane, podziwa kuti ali munthu wolungama ndi woyera mtima, ndipo anamsunga iye. Ndipo pamene anamva iye anathedwa nzeru, nakondwa kumva iye.


Ndipo za pathanthwe ndiwo amene, pakumva, alandira mau ndi kukondwera; koma alibe mizu; akhulupirira kanthawi, ndipo pa nthawi ya mayesedwe angopatuka.


Mutengenso chisoti cha chipulumutso, ndi lupanga la Mzimu, ndilo Mau a Mulungu;


Ndi chikhulupiriro tizindikira kuti maiko ndi a m'mwamba omwe anakonzedwa ndi mau a Mulungu, kotero kuti zinthu zopenyeka sizinapangidwe kuchokera mu zoonekazo.


Pakuti sanagonjetsere angelo dziko lilinkudza limene tinenali.


Pakuti mau a Mulungu ali amoyo, ndi ochitachita, ndi akuthwa koposa lupanga lakuthwa konsekonse, napyoza kufikira kugawira moyo ndi mzimu, ndi zimfundo ndi mafuta a m'mafupa, nazindikiritsa zolingirira ndi zitsimikizo za mtima.


koma Mau a Ambuye akhala chikhalire. Ndipo mau olalikidwa kwa inu ndi awo.


ngati mwalawa kuti Ambuye ali wokoma mtima;


Pakuti ngati, adatha kuthawa zodetsa za dziko lapansi mwa chizindikiritso cha Ambuye ndi Mpulumutsi Yesu Khristu, akondwanso nazo, nagonjetsedwa, zotsiriza zao zidzaipa koposa zoyambazo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa