Ahebri 5:5 - Buku Lopatulika5 Koteronso Khristu sanadzilemekeze yekha ayesedwe Mkulu wa ansembe, komatu Iye amene analankhula kwa Iye, Mwana wanga ndi Iwe, lero Ine ndakubala Iwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Koteronso Khristu sanadzilemekeza yekha ayesedwe Mkulu wa ansembe, komatu Iye amene analankhula kwa Iye, Mwana wanga ndi Iwe, lero Ine ndakubala Iwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Momwemonso Khristu sadadzikweze yekha ku ulemu wokhala mkulu wa ansembe onse, koma Mulungu ndiye adachita kumuuza kuti, “Iwe ndiwe Mwana wanga, Ine lero ndakubala.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Nʼchifukwa chake Khristu sanadzipatse yekha ulemu wokhala Mkulu wa ansembe. Koma Mulungu anamuwuza kuti, “Iwe ndiwe Mwana wanga; Ine lero ndakhala Atate ako.” Onani mutuwo |