Ahebri 5:6 - Buku Lopatulika6 Monga anenanso mwina, Iwe ndiwe wansembe wa nthawi zonse monga mwa dongosolo la Melkizedeki. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Monga anenanso mwina, Iwe ndiwe wansembe wa nthawi zonse monga mwa dongosolo la Melkizedeki. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Penanso Mulungu adati, “Ndiwe wansembe mpaka muyaya, unsembe wake wonga uja wa Melkizedeki.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Ndipo penanso anati, “Iwe ndiwe wansembe mpaka muyaya, monga mwa unsembe wa Melikizedeki.” Onani mutuwo |