Ahebri 5:3 - Buku Lopatulika3 ndipo chifukwa chakecho ayenera, monga m'malo a anthuwo, moteronso m'malo a iye yekha, kupereka nsembe chifukwa cha machimo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 ndipo chifukwa chakecho ayenera, monga m'malo a anthuwo, moteronso m'malo a iye yekha, kupereka nsembe chifukwa cha machimo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Nchifukwa chake aumirizidwa kumapereka nsembe chifukwa cha machimo a iye yemwe, ndiponso machimo a anthu ena. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Chifukwa cha ichi, iye amadziperekera nsembe chifukwa cha machimo ake omwe ndiponso chifukwa cha machimo a anthu ena. Onani mutuwo |