Ahebri 5:2 - Buku Lopatulika2 akhale wokhoza kumva chifundo ndi osadziwa ndi olakwa, popeza iye yekhanso amazingwa ndi chifooko; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 akhale wokhoza kumva chifundo ndi osadziwa ndi olakwa, popeza iye yekhanso amazingwa ndi chifooko; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Popeza kuti iye yemweyo ali ndi zofooka zambiri, ndiye kuti angathe kuŵalezera mtima amene ali opanda nzeru ndi osokera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Popeza kuti iye mwini ali ndi zofowoka zake, amatha kuwalezera mtima amene ali osadziwa ndi osochera. Onani mutuwo |