Ahebri 5:13 - Buku Lopatulika13 Pakuti yense wakudya mkaka alibe chizolowezi cha mau a chilungamo; pakuti ali khanda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Pakuti yense wakudya mkaka alibe chizolowezi cha mau a chilungamo; pakuti ali khanda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Ngati wina aliyense angomwa mkaka, ndiye kuti akali mwana wakhanda, sangathe kutsata chiphunzitso chofotokoza za chilungamo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Aliyense amene amangodya mkaka okha, akanali mwana wakhanda, sakudziwa bwino chiphunzitso cha chilungamo. Onani mutuwo |