Ahebri 4:9 - Buku Lopatulika9 Momwemo utsalira mpumulo wa Sabata wa kwa anthu a Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Momwemo utsalira mpumulo wa Sabata wa kwa anthu a Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Nchifukwa chake tsono mpumulo wonga wa pa Sabata waŵatsalirabe anthu a Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Kotero tsono kwatsala mpumulo wa Sabata kwa anthu a Mulungu; Onani mutuwo |