Ahebri 4:10 - Buku Lopatulika10 Pakuti iye amene adalowa mpumulo wake, adapumulanso mwini wake kuntchito zake, monganso Mulungu kuzake za Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Pakuti iye amene adalowa mpumulo wake, adapumulanso mwini wake kuntchito zake, monganso Mulungu kuzake za Iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Paja munthu woloŵa mu mpumulo umene Mulungu adalonjeza, nayenso amapumula, kuleka ntchito zake, monga momwe Mulungu adaapumulira, kuleka ntchito zake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Pakuti aliyense amene analowa mu mpumulo wa Mulungu anapuma pa ntchito zake, monga momwe Mulungu anachitira. Onani mutuwo |