Ahebri 4:11 - Buku Lopatulika11 Chifukwa chake tichite changu cha kulowa mpumulowo, kuti wina angagwe m'chitsanzo chomwe cha kusamvera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Chifukwa chake tichite changu cha kulowa mpumulowo, kuti wina angagwe m'chitsanzo chomwe cha kusamvera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Tiyesetse tsono kuloŵa mu mpumulowo, kuwopa kuti wina aliyense angakhale wosamvera monga iwo aja, nalephera kuloŵamo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Tiyeni tsono tiyesetse kulowa mu mpumulo, kuti pasapezeke wina aliyense wolephera potsatira chitsanzo chawo cha kusamvera. Onani mutuwo |