Ahebri 4:8 - Buku Lopatulika8 Pakuti ngati Yoswa akadawapumitsa iwo, sakadalankhula m'tsogolomo za tsiku lina. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Pakuti ngati Yoswa akadawapumitsa iwo, sakadalankhula m'tsogolomo za tsiku lina. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Chifukwatu Yoswa akadaŵaloŵetsa anthuwo mu mpumulo uja, sibwenzi pambuyo pake atanena za tsiku linanso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Ngati Yoswa akanalowetsa anthu mu mpumulo, Mulungu sakananena pambuyo pake za tsiku lina. Onani mutuwo |