Ahebri 4:6 - Buku Lopatulika6 Popeza tsono patsala kuti ena akalowa momwemo, ndi iwo amene Uthenga Wabwino unalalikidwa kwa iwo kale sanalowemo chifukwa cha kusamvera, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Popeza tsono patsala kuti ena akalowa momwemo, ndi iwo amene Uthenga Wabwino unalalikidwa kwa iwo kale sanalowamo chifukwa cha kusamvera, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Mulungu adakonza kuti ena aloŵe ndithu mu mpumulowo, koma aja adaamva Uthenga Wabwino poyambaŵa sadaloŵemo chifukwa cha kusamvera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Popeza kwatsalabe kuti ena adzalowe mu mpumulowo, koma aja anayamba kumva Uthenga Wabwino sanalowe chifukwa cha kusamvera kwawo. Onani mutuwo |