Ahebri 4:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo m'menemonso, Ngati adzalowa mpumulo wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo m'menemonso, Ngati adzalowa mpumulo wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Panonso akunena za zomwezo pamene akuti, “Sadzaloŵa konse mu mpumulo umene ndidaŵakonzera.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Pa ndime inonso akunena za zomwezo pamene akuti, “Iwo sadzalowa konse mu mpumulo wanga.” Onani mutuwo |