Ahebri 3:8 - Buku Lopatulika8 musaumitse mitima yanu, monga m'kupsetsa mtimamo, monga muja tsiku la chiyesero m'chipululu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 musaumitse mitima yanu, monga m'kupsetsa mtimamo, monga muja tsiku la chiyesero m'chipululu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 musaumitse mitima yanu monga muja zidaachitikira pomuukira Mulungu, tsiku la kumuyesa m'chipululu muja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 musawumitse mitima yanu ngati munachitira pamene munawukira, pa nthawi yoyesedwa mʼchipululu. Onani mutuwo |